1
Luka 24:49
Nyanja
NTNYBL2025
Ine sinikutumileni uyo ahidi Atate wanga, nambho muyendekele kulindilila muno mu Yelusalemu mbaka yapo simulandile mbhavu kuchokela kumwamba.”
ប្រៀបធៀប
រុករក Luka 24:49
2
Luka 24:6
Iye palibepo pano, wahyuka. Mkumbukile umo wadakambila yapo wadali pamojhi ni anyiimwe kujha ku Galilaya
រុករក Luka 24:6
3
Luka 24:31-32
Ndhawi imweyo maso yawo yadamasuka, adamjhiwa kuti ni Yesu, ni iye wadasowa pakati pawo. Ndiipo adafunjhana, “Bwanji, mitima yathu siimakwelele kwa kukondwela yapo wamakamba niife ni kutifotokozela malembo mnjila mujha?”
រុករក Luka 24:31-32
4
Luka 24:46-47
Wadakambila, “Yadalembedwa yaya mu malembo Yoyela kuti, Kilisito Muomboli siwavutike ni kumwalila, siku la katatu siwahyuke, nikuti wandhu amayiko yonjhe kuyambila Yelusalemu, alalikidwe kwa jhina la Yesu kuti alape, ni kulekeleledwa machimo.
រុករក Luka 24:46-47
5
Luka 24:2-3
Yapo adafika kumanda, adakomana mwala ujha waukulu lagunghulichidwa kutali ni pakhomo chiliza. Nambho yapo adalowa mkati mwa chiliza, sadalipheze chitanda la Ambuye Yesu.
រុករក Luka 24:2-3
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ