Luka 24:31-32
Luka 24:31-32 NTNYBL2025
Ndhawi imweyo maso yawo yadamasuka, adamjhiwa kuti ni Yesu, ni iye wadasowa pakati pawo. Ndiipo adafunjhana, “Bwanji, mitima yathu siimakwelele kwa kukondwela yapo wamakamba niife ni kutifotokozela malembo mnjila mujha?”