1
Alom 6:23
Nyanja
NTNYBL2025
Pakuti ukayatumikila machimo siufe, nambho mbhaso iyo wachocha Mnungu ni umoyo wa muyaya kwa kulunjana ni Kilisito Yesu, Ambuye wathu.
ប្រៀបធៀប
រុករក Alom 6:23
2
Alom 6:14
Machimo siyakulamulilani njhoni, pakuti anyiimwe simchogozedwa ni thauko, nambho mchogozedwa ni ubwino.
រុករក Alom 6:14
3
Alom 6:4
Yapo tidabatizidwa tidalunjana ni nyifa yake, tidazikidwa pamojhi niiye, kuti ngati mujha kilisito wadahyukichidwa kwa mbhavu yaikulu ya Atate, ife nafe tikhoze kukhala ni umoyo wa chipano.
រុករក Alom 6:4
4
Alom 6:13
Msidachichita chiwalo chilichonjhe cha matupi yanu kuhala chindhu cho chitila machimo. Pambuyo pake jhichocheni mwachinawenewake kwa Mnungu ngati wandhu mwa hyuka, vichocheni viwalo vanu kwa Mnungu ngati vindhu ivo vavomelezeka.
រុករក Alom 6:13
5
Alom 6:6
Tijhiwa kuti vichito vathu va kale vidafa ni vidapachikidwa pa mtanda pamojhi niiye, kuti mbhavu za machimo ziwanangidwe, ni sitidakhalanjho akapolo a machimo.
រុករក Alom 6:6
6
Alom 6:11
Chinchijha anyiimwe ifunika mjhione kuti mwafa kwa nghani ya machimo, nambho ngati mkhala kwa umojhi ni Mnungu kwa kumkhulupilila Yesu Kilisito.
រុករក Alom 6:11
7
Alom 6:1-2
Tikambe chiyani chipano? Bwanji tiendekele kukhala mmachimo kuti ubwino wa Mnungu uchuluke? Notho! Ife tayafela machimo, sitiendekele bwanji kukhala mmachimo?
រុករក Alom 6:1-2
8
Alom 6:16
Mjhiwa kuti anyiiwe mkajhichocha mwachina wene ngati akapolo wa mundhu waliyonjhe mkhala akapolo azene amundhu yujha, ni ngati mkachichocha kukhla akapolo wa machimo mathelo yake ni nyifa, nambho mkachichocha kumvela Mnungu simkhale ovemelezeka kwa Mnungu?
រុករក Alom 6:16
9
Alom 6:17-18
Nambho chipano nimuyamika Mnungu, pakuti anyiimwe kale mdali akapolo amachimo, mwakhala ovela kwa mtima yanu yonjhe kwa mayaluzo mdayaluzidwa. Mdaomboledwa kuchokela kuukapolo wa machimo, chipano mwakhala akapolo akuchita yajha yamkwadilicha Mnungu.
រុករក Alom 6:17-18
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ