Mk. 5:8-9

Mk. 5:8-9 BLY-DC

Adaatero chifukwa Yesu anali atanena kuti, “Mzimu woipawe, tuluka mwa munthuyu!” Tsono Yesu adamufunsa munthuyo kuti, “Dzina lako ndani?” Iye adayankha kuti, “Dzina langa ndine ‘Chigulu,’ chifukwa tilipo ochuluka.”

مطالعه Mk. 5

ویدیوهای مرتبط

برنامه های خواندنی رایگان و عبادات مربوط به Mk. 5:8-9