Alom 6
6
Kumwalila mmachimo ni kukhala kwa kilisito
1Tikambe chiyani chipano? Bwanji tiendekele kukhala mmachimo kuti ubwino wa Mnungu uchuluke? 2Notho! Ife tayafela machimo, sitiendekele bwanji kukhala mmachimo? 3Mjhiwa ife tidabatizidwa tidalunjana ni Yesu Kilisito, tidabatizidwa ni kulunjana ni nyifa yake. 4Yapo tidabatizidwa tidalunjana ni nyifa yake, tidazikidwa pamojhi niiye, kuti ngati mujha kilisito wadahyukichidwa kwa mbhavu yaikulu ya Atate, ife nafe tikhoze kukhala ni umoyo wa chipano.
5Pakuti ife talunjana niiye kwa njila nyifa yake, chimwecho ife sitilunjane naye kwa kuhyukichidwa ngati iye. 6Tijhiwa kuti vichito vathu va kale vidafa ni vidapachikidwa pa mtanda pamojhi niiye, kuti mbhavu za machimo ziwanangidwe, ni sitidakhalanjho akapolo a machimo. 7Mundhu wakafa kwa mtundu umeneo siwakhaliletu hulu kuchokela mmbhavu za machimo. 8Chipano, tamwalila pamojhi ni Kilisito, tikhulupilila kuti sitikhale pamojhi niiye. 9Chipano tijhiwa Kilisito watohyukichidwa siwamwalilanjho ni nyifa simlamulanjho. 10Chimwecho pakuti wadamwalila mala kamojhipe ni wadaikoza mbhavu ya machimo, sazino ni wamoyo ni paumoyo wake wamkwadilicha Mnungu, 11Chinchijha anyiimwe ifunika mjhione kuti mwafa kwa nghani ya machimo, nambho ngati mkhala kwa umojhi ni Mnungu kwa kumkhulupilila Yesu Kilisito.
12Chipano machimo siyadalamulanjho wiwalo va matupi yanu yayo siyafe, ni siyadakuchitani muyavele makumbilo yanu. 13Msidachichita chiwalo chilichonjhe cha matupi yanu kuhala chindhu cho chitila machimo. Pambuyo pake jhichocheni mwachinawenewake kwa Mnungu ngati wandhu mwa hyuka, vichocheni viwalo vanu kwa Mnungu ngati vindhu ivo vavomelezeka. 14Machimo siyakulamulilani njhoni, pakuti anyiimwe simchogozedwa ni thauko, nambho mchogozedwa ni ubwino.
Akapolo akuchita yayo yamkwadilicha Mnungu
15Chipano tikambe chiyani? Tichite machimo ndande sitichogozedwa ni thauko nambho tichochogozwedwa ni ubwino? Notho! 16Mjhiwa kuti anyiiwe mkajhichocha mwachina wene ngati akapolo wa mundhu waliyonjhe mkhala akapolo azene amundhu yujha, ni ngati mkachichocha kukhla akapolo wa machimo mathelo yake ni nyifa, nambho mkachichocha kumvela Mnungu simkhale ovemelezeka kwa Mnungu? 17Nambho chipano nimuyamika Mnungu, pakuti anyiimwe kale mdali akapolo amachimo, mwakhala ovela kwa mtima yanu yonjhe kwa mayaluzo mdayaluzidwa. 18Mdaomboledwa kuchokela kuukapolo wa machimo, chipano mwakhala akapolo akuchita yajha yamkwadilicha Mnungu. 19Nakamba ni anyiiimwe kwa kutumia mkambo uno wa akapolo kuti mkoze kujhiwa icho nakamba, kale mdali akapolo a machimo kwa kujhichocha mwachinawene kukhala vindhu vochita vindhu voipa ni machimo yanu yadali yambili kupunda, nambho saino ifunika mjhichoche kwa mnungu pa umoyo wanu wonjhe. Mkhale akapolo kwa vindhu ivo vimkwadilicha Mnungu. Mjhichita vindhu vavomelezeka ni Mnungu mwene kulangiza kuti anyiimwe ni wandhu wa Amnungu.
20Kale mdali akapolo amachimo, simdaganizile kuchita vindhu ivo vimkwadilicha Mnungu. 21Chipano mdapata chiyani siku zijha kuchokana ni vindhu vijha mvionela njhoni saino? Pakuti vindhu ivi vipeleka nyifa! 22Nambho saino mwalekeleledwa kuchokela ku ukapolo wa machimo, ni mwakhala akapolo a Mnungu, mwakhala wandhu wake ni mathelo yake simpate umoyo wa muyaya. 23Pakuti ukayatumikila machimo siufe, nambho mbhaso iyo wachocha Mnungu ni umoyo wa muyaya kwa kulunjana ni Kilisito Yesu, Ambuye wathu.
ទើបបានជ្រើសរើសហើយ៖
Alom 6: NTNYBL2025
គំនូសចំណាំ
ចែករំលែក
ចម្លង
ចង់ឱ្យគំនូសពណ៌ដែលបានរក្សាទុករបស់អ្នក មាននៅលើគ្រប់ឧបករណ៍ទាំងអស់មែនទេ? ចុះឈ្មោះប្រើ ឬចុះឈ្មោះចូល
The New Testament in Nyanja @The Word for The World International and Nyanja Language translation, 2025. All rights reserved.
Alom 6
6
Kumwalila mmachimo ni kukhala kwa kilisito
1Tikambe chiyani chipano? Bwanji tiendekele kukhala mmachimo kuti ubwino wa Mnungu uchuluke? 2Notho! Ife tayafela machimo, sitiendekele bwanji kukhala mmachimo? 3Mjhiwa ife tidabatizidwa tidalunjana ni Yesu Kilisito, tidabatizidwa ni kulunjana ni nyifa yake. 4Yapo tidabatizidwa tidalunjana ni nyifa yake, tidazikidwa pamojhi niiye, kuti ngati mujha kilisito wadahyukichidwa kwa mbhavu yaikulu ya Atate, ife nafe tikhoze kukhala ni umoyo wa chipano.
5Pakuti ife talunjana niiye kwa njila nyifa yake, chimwecho ife sitilunjane naye kwa kuhyukichidwa ngati iye. 6Tijhiwa kuti vichito vathu va kale vidafa ni vidapachikidwa pa mtanda pamojhi niiye, kuti mbhavu za machimo ziwanangidwe, ni sitidakhalanjho akapolo a machimo. 7Mundhu wakafa kwa mtundu umeneo siwakhaliletu hulu kuchokela mmbhavu za machimo. 8Chipano, tamwalila pamojhi ni Kilisito, tikhulupilila kuti sitikhale pamojhi niiye. 9Chipano tijhiwa Kilisito watohyukichidwa siwamwalilanjho ni nyifa simlamulanjho. 10Chimwecho pakuti wadamwalila mala kamojhipe ni wadaikoza mbhavu ya machimo, sazino ni wamoyo ni paumoyo wake wamkwadilicha Mnungu, 11Chinchijha anyiimwe ifunika mjhione kuti mwafa kwa nghani ya machimo, nambho ngati mkhala kwa umojhi ni Mnungu kwa kumkhulupilila Yesu Kilisito.
12Chipano machimo siyadalamulanjho wiwalo va matupi yanu yayo siyafe, ni siyadakuchitani muyavele makumbilo yanu. 13Msidachichita chiwalo chilichonjhe cha matupi yanu kuhala chindhu cho chitila machimo. Pambuyo pake jhichocheni mwachinawenewake kwa Mnungu ngati wandhu mwa hyuka, vichocheni viwalo vanu kwa Mnungu ngati vindhu ivo vavomelezeka. 14Machimo siyakulamulilani njhoni, pakuti anyiimwe simchogozedwa ni thauko, nambho mchogozedwa ni ubwino.
Akapolo akuchita yayo yamkwadilicha Mnungu
15Chipano tikambe chiyani? Tichite machimo ndande sitichogozedwa ni thauko nambho tichochogozwedwa ni ubwino? Notho! 16Mjhiwa kuti anyiiwe mkajhichocha mwachina wene ngati akapolo wa mundhu waliyonjhe mkhala akapolo azene amundhu yujha, ni ngati mkachichocha kukhla akapolo wa machimo mathelo yake ni nyifa, nambho mkachichocha kumvela Mnungu simkhale ovemelezeka kwa Mnungu? 17Nambho chipano nimuyamika Mnungu, pakuti anyiimwe kale mdali akapolo amachimo, mwakhala ovela kwa mtima yanu yonjhe kwa mayaluzo mdayaluzidwa. 18Mdaomboledwa kuchokela kuukapolo wa machimo, chipano mwakhala akapolo akuchita yajha yamkwadilicha Mnungu. 19Nakamba ni anyiiimwe kwa kutumia mkambo uno wa akapolo kuti mkoze kujhiwa icho nakamba, kale mdali akapolo a machimo kwa kujhichocha mwachinawene kukhala vindhu vochita vindhu voipa ni machimo yanu yadali yambili kupunda, nambho saino ifunika mjhichoche kwa mnungu pa umoyo wanu wonjhe. Mkhale akapolo kwa vindhu ivo vimkwadilicha Mnungu. Mjhichita vindhu vavomelezeka ni Mnungu mwene kulangiza kuti anyiimwe ni wandhu wa Amnungu.
20Kale mdali akapolo amachimo, simdaganizile kuchita vindhu ivo vimkwadilicha Mnungu. 21Chipano mdapata chiyani siku zijha kuchokana ni vindhu vijha mvionela njhoni saino? Pakuti vindhu ivi vipeleka nyifa! 22Nambho saino mwalekeleledwa kuchokela ku ukapolo wa machimo, ni mwakhala akapolo a Mnungu, mwakhala wandhu wake ni mathelo yake simpate umoyo wa muyaya. 23Pakuti ukayatumikila machimo siufe, nambho mbhaso iyo wachocha Mnungu ni umoyo wa muyaya kwa kulunjana ni Kilisito Yesu, Ambuye wathu.
ទើបបានជ្រើសរើសហើយ៖
:
គំនូសចំណាំ
ចែករំលែក
ចម្លង
ចង់ឱ្យគំនូសពណ៌ដែលបានរក្សាទុករបស់អ្នក មាននៅលើគ្រប់ឧបករណ៍ទាំងអស់មែនទេ? ចុះឈ្មោះប្រើ ឬចុះឈ្មោះចូល
The New Testament in Nyanja @The Word for The World International and Nyanja Language translation, 2025. All rights reserved.