Alom 2

2
Lamulo la Mnungu
1Bwenji, ngati iwe waalamula wina, siukhoza kulama ata ngati iwe ni yani. Pakuti ngati waalamula wina, ni iwe umwene wake uchita vinvijha waalamulila wina nawenjho siulamulidwe. 2Tijhiwa kuti lamulo la Mnungu kwa wandhu achita vindhu ngati vimenevo ni lamulo la uzene. 3Nambho iwe ulamula wandhu yawo achita vindhu voipa ngati umo uchitila umwene, uganiza kuti ukhoza kulithawa lamulo la Mnungu? 4Kapina upepula kuchuluka kwa ubwino wake waukulu, kulimba kwake mtima ni kulindilila kwake, siujhiwa kuti ubwino wake umenewo uli ni ndande ya kukuchogoza iwe kuti ulape? 5Nambho iwe siuvela ukana kusiya machimo, mumchita Mnungu kuti wakwiye kupunda yapo siwajhe kulamula pa siku la lamulo lake. 6Siku limenelo Mnungu siwakulamuleni kwa kukalipa kila mundhu kuchokana ni vichito vake. 7Anyiwajha ayembekeza kuchita vabwino kufunafuna ulemelelo ni ulemu wa Mnungu, ni umoyo uwo siuwanangika Mnungu siwapache umoyo wa muyaya. 8Nambho anyiwajha achata vindhu vao achina wene, ni anyiwajha akana uzene ni kuchata njila zoipa, Mnungu siwakwiile ni kwaalanga kwa mbhwayi. 9Mnungu siwamlange waliyonjhe uyo wachita voipa. Siyapate Ayahudi uti ni wandhu a maiko yina 10Nambho Mnungu siwachite aelekeledwe, siwapache ulemu ni mtendele anyiwajha achita vabwino, Ayahudi uti ni wandhu amaiko yina. 11Pakuti Mnungu siwamlamula mundhu waliyonjhe kwa kukondelela.
12Wandhu wonjhe osati Ayahudi achita machimo popande kulijhiwa thauko la Mnungu ilo wadampacha Musa, sayomwe ata ngati sadalijhiwe thauko limenelo. Chimwecho anyiwajha achita machimo uku ni alijhiwa thauko, sialamulidwe kuchokana ni umo likambila thauko. 13Pakuti osati anyiwajha alivela thauko nde savomelezeke kuti achita va bwino kwa Mnungu. Nambho anyiwajha achata thauko nde savomelezeke kuti achita vabwino kwa Mnungu. 14Pakuti wandhu osati Ayahudi alibe thauko, kila yapo achita icho chifuna thauko uku ni achogozedwa ni mitima yao, anyiiwo akhala thauko ata ngati sialijhiwa thauko. 15Ukhalo wao ulangiza kuti chijha chifunika ni thauko chalembedwa mmitima mwao, ni mitima yao ikambilila chindhu chimenecho, ni pakuti maganizo yao ndhawi ina yapacha mlandu, ni ndhawi ina yaimila. 16Chimwecho, kuchokana ni uwu Uthenga wa Bwino uwo nilalikila, ndeumo sikhalile ndhawi iyo Mnungu siwalamule vindhu va chisisi va wandhu kwa njila ya Yesu kilisito.
Ayahudi ni thauko la Mnungu
17Niiwe ujhitana Myahudi, ulikhulupila thauko ni uchita dama kuti iwe ni mundhu wa Mnungu, 18ngati ujhiwa icho wachifuna Mnungu ni kuvomela icho chili chabwino, ndande wayaluzidwa ni thauko limenelo. 19Iwe ujhiwa kuti ukhoza kwayaluza wandhu osapenya nghani za Mnungu, ni kwachogoza wandhu yawo sapenya, ni kwapacha dangalila anyiwajha ali mumdima, 20ujhiwa kuti uyaluza asabwabwa ni anyiwajha sadaujhiwe uzene wa chikhulupililo. Ujhiwa kuti thauko la Mnungu likamba uzene wonjhe wa nghani za Mnungu 21Chipano iwe uyaluza wina ndande yanji siudajhiyaluza umwene? Walalikila wina sadaba nambho wamwene ukuba. 22Ukamba, “Simdachita chigololo” uku wamwene uchita chigololo, uipila viboliboli va minungu ni wamwene ukuba vindhu va mnyumba ya minungu. 23Ujhidama kuti ulijhiwa thauko la Mnungu, nambho umdelela Mnungu kwa kuliwananga thauko lake? 24Ngati mujha yalembedwa mmalembo yoyela, “Ndande ya vichito vanu voipa Wandu amaiko yina, amtukwana Mnungu”
25Kuchita kwako mdulidwe sikukhale ni mate ngati siuchate thauko, nambho ngati siuchata thauko, mbasa udakakhala popande kuchita mdulidwe. 26Ngati mundhu wa mayiko yina uyo siwadachitidwe mdulidwe, wakachita ngati umo wafunila Mnungu, siwawelengedwe kuti wachitidwa mdulidwe. 27Wandhu amaiko yina sakulamule iwe Muyahudi ngati siuchata thauko, ata ngati uli ni malembo ya thauko ni wachitidwa mdulidwe, pakuti anyiiwo alichata thauko atangati sadachitidwe mdulidwe. 28Pakuti osati kila mundhu uyo wabadwa ni Muyahudi nde Muyahudi wa zene, ni mundhu siwakhala Muyahudi wazene ndande wachitidwa mdulidwe chithupi. 29Muyahudi wa zene ni yujha wali Myahudi kwa mkati, yani yujha mundhu wachitidwa mdulidwe mu mtima, ichi ni chindhu cha chizimu, osati chindhu cha malembo ya thauko. Mundhu wa mtundu umeneo waelekeledwa, osati ni wandhu nambho ni Mnungu.

ទើបបានជ្រើសរើសហើយ៖

Alom 2: NTNYBL2025

គំនូស​ចំណាំ

ចែក​រំលែក

ចម្លង

None

ចង់ឱ្យគំនូសពណ៌ដែលបានរក្សាទុករបស់អ្នក មាននៅលើគ្រប់ឧបករណ៍ទាំងអស់មែនទេ? ចុះឈ្មោះប្រើ ឬចុះឈ្មោះចូល