Luka 19:5-6
Luka 19:5-6 NTNYBL2025
Yesu yapo wadafika pamalo yameneyo, wadapenya mmwamba mwa mtengo ni kumkambila, “Zakayo, chika chisanga, pakuti lelo sinikhale mlendo kukhomo lako.” Zakayo wadachika chisanga ni kumlandila Yesu kwa kukondwela.
Yesu yapo wadafika pamalo yameneyo, wadapenya mmwamba mwa mtengo ni kumkambila, “Zakayo, chika chisanga, pakuti lelo sinikhale mlendo kukhomo lako.” Zakayo wadachika chisanga ni kumlandila Yesu kwa kukondwela.