Luka 19:39-40
Luka 19:39-40 NTNYBL2025
Afalisayo wina yawo adali mkati mwa gulu lijha, yapo adaona chimwecho, adamkambila Yesu, “Oyaluza, anyindileni oyaluzidwa wanu akhale chete!” Yesu wadayangha, “Nikukambilani kuti, ngati anyiyawa saakhale chete, miyala siibule phokoso.”