Vichito 22
22
1Poolo wadakamba achaabale wanga ni anyaatate wanga munivele bwino umo nijhiteteza pachogolo panu! 2Yapo adamvela niwaakambila mu Chihebulaniya, adapunda kukhala chete, ni Poolo wadayendekela kukamba,
3“Ine ni Muyahudi, nidabadwila ku Taliso mmujhi wa Kilikiya. Nambho nakulilila muno mu Yelusalemu ine ni oyaluzidwa wa Gamalieli. Nidayaluzidwa kuchata mokwana Thauko la azee wathu akale. Nidajhichocha mwa mtima wanga wojhe kwa Mnungu ngati umo mwajhichochochela anyiimwe pano. 4Nidavuticha ni kwa ipha wandhu wajha adachata njila ya ukhalo uwu. Nidaagwila wachimuna ni wachikazi ni kwamanga mndende. 5Mjhukulu wamkulu ni bwalo lonjhe la azee Achiyahudi akhoza kukuchimikizilani nghani izi. Kuchokela kwanyiiwo nidalandila kalata iyo idalembedwa ni wajha abale a Chiyahudi aku Damasiko, ni nidapita kujha kwaagwila wandhu ni kujhanawo ku Yelusalemu uku amangidwa maunyolo kuti alangidwe.”
Poolo wakamba umo Yesu wadamtulukila
Vichito 9:1-19; 26:12-18
6“Chimwecho yapo nidali paulendo pafupi kufika ku damasiko, ngati sasita usana chimwechi, dangalila long'azimila kupunda kuchokela kumwamba lidaniwalila kunizungulila madela yonjhe mwachizulumukila. 7Nidagwa panjhi ni nidavela mvekelo niunikambila, ‘Saulo, Saulo! Ndande yanji univuticha?’ 8Nidayangha, ‘Imwe ayani, Ambuye?’ Mvekelo udaveka, ‘Ine Yesu wa ku Nazaleti, uyo univuticha.’ 9Wandhu yawo adali niine adaliona dangalila, nambho saadauvele mvekelo wa uyo wamakamba nane. 10Ndiipo nidafunjha, ‘Ifunika nichite chiyani, Ambuye?’ Ambuye adaniyangha, ‘Ima ni upite ku Damasiko. Kumeneko sinikukambile yonjhe yayo Mnungu waikilidwa uyachite.’ 11Nidali wosapenya ndande ya lijha dangalila lalikulu lidaniwalila, ni athandizi wanga adanigwila jhanja ni kupita nane ku Damasiko.”
12“Kujha ku Damasiko kudali mundhu uyo wamatanidwa Ananiya, mundhu uyo wagwila thauko ni wamalemekezedwa ni Ayahudi wonjhe yawo amakhala ku damesiko. 13Iye wadajha kwa ine, wadaima pafupi ni ine ni kukamba, ‘Mbale wanga Saulo, penyanjho!’ Pampajha maso yanga yadayamba kupenyanjho nane nidamuona Ananiya. 14Wadakamba, ‘Mnungu wa achaatate wathu wakusangha iwe kuti ujhiwe vindu ivo avifuna uchite. Wakusangha iwe kuti umuone Mtumiki wake ni kumvela iye. 15Pakuti iwe siwakambile wandhu yajha wayaona ni kuyavela. 16Chipano siufunika kulindila ndhawi yaitali. Ima ubatizidwe ni kuelechedwa machimo yako dala ulekeleledwe kwa kukhulupilila jhina la Ambuye.’”
Ambuye amtuma Poolo kwaalalikila wandhu osati Ayahudi
17“Nidabwelela ku Yelusalemu, nambho yapo nidalikupembhela pa Nyumba ya Mnungu, nidaona masombhenya. 18Nidaaona Ambuye, uku nianikambila, ‘Uchite msanga uchoke mu Yelusalemu, pakuti wandhu anyiyawa saaulandila umboni wanga uwo siuchoche.’ 19Ine nidayangha, ‘Ambuye, anyiiwo ajhiwa bwino kuti nidapita mmanyumba yonjhe yokomanilana Ayahudi ni kwaabula yawo akukhulupililani imwe. 20Yapo wamaphedwa Sitifano mmboni wako, ine namwene nidali pampajha ni nidavomelezana kuti wapedwe niine nde nimalonda njhalu zawajha akupha’ 21Ambuye adanikambila, ‘Pita, pakuti sinikutume kutali kwa wandhu osati Ayahudi.’”
22Mbaka yapa, wajha wandhu amamvechela, nambho yapo wadakamba mawu yaya, ndiipo adakweza mvekelo wao niakamba mundhu mmeneyo waphedwe mundhu, ndande yake siwafunika kukhala wamoyo! 23Anyiiwo amabula phokoso ni kuvula njhalu zao ni kufulila lifumbi kumwamba. 24Ndiipo yujha wamkulu wa asikali wadalamula kuti amgwile Poolo ni kumlovya mkati mwa nyumba ya asikali, niwadalamula kuti wabulidwe mikwapulo, uku niwamfujha ndande yanjhi Ayahudi abula pokoso. 25Nambho yapo adathommanga vingwe kuti amkwapule, Poolo wadamfunjha mkulu wa gulu la asikali uyo wadaima pampajha pafupi ni iye, “Bwanji, thauko la jhiko la Aloma lilola kumbula mundhu wakuloma wakali osalamulidwe?”
26Wamkulu yujha yapo wadavela chimwechi, wadapita kwa wamkulu wa asikali ni kumkambila, “Ufuna kuchita chiyani? Uyu mundhu ni Mloma!”
27Chimwecho wamkulu wa asikali yujha wathamangila kwa Poolo ni kumfunjha, “Nikambile, iwe ni mundhu wa ku Loma?”
Poolo wadayangha, “Yetu, ine mundhu wa ku Loma.”
28Wamkulu wa asikali wadakamba, “Ine nane ni Mloma kwa kulipila ndalama zambili.”
Poolo wadayangha, “Nambho ine ni Mloma wobadwa.”
29Kankamojhi wandhu wajha amafuna kumfunjha uku ni ambula, pampajha adachoka ni yujha wamkulu wa asikali wadaopa kupunda yapo wadajhiwa kuti Poolo wadali Mloma wadaopa ndande wadathommanga maunyolo.
Poolo wapelekedwa pa bwalo la milandu
30Siku lakawili wamkulu wa asikali wamafuna kujhiwa ndande iyo Ayahudi amafuna kumpacha mlandu Poolo. Chimwecho wadammasula yajha maunyolo ni wadalamula ajhukulu wakulu na azee a bwalo lalikulu lonjhe kukomana pamojhi. Ndiipo wadamtenga Poolo ni kumuika waime pachogolo pao.
ទើបបានជ្រើសរើសហើយ៖
Vichito 22: NTNYBL2025
គំនូសចំណាំ
ចែករំលែក
ចម្លង
ចង់ឱ្យគំនូសពណ៌ដែលបានរក្សាទុករបស់អ្នក មាននៅលើគ្រប់ឧបករណ៍ទាំងអស់មែនទេ? ចុះឈ្មោះប្រើ ឬចុះឈ្មោះចូល
The New Testament in Nyanja @The Word for The World International and Nyanja Language translation, 2025. All rights reserved.
Vichito 22
22
1Poolo wadakamba achaabale wanga ni anyaatate wanga munivele bwino umo nijhiteteza pachogolo panu! 2Yapo adamvela niwaakambila mu Chihebulaniya, adapunda kukhala chete, ni Poolo wadayendekela kukamba,
3“Ine ni Muyahudi, nidabadwila ku Taliso mmujhi wa Kilikiya. Nambho nakulilila muno mu Yelusalemu ine ni oyaluzidwa wa Gamalieli. Nidayaluzidwa kuchata mokwana Thauko la azee wathu akale. Nidajhichocha mwa mtima wanga wojhe kwa Mnungu ngati umo mwajhichochochela anyiimwe pano. 4Nidavuticha ni kwa ipha wandhu wajha adachata njila ya ukhalo uwu. Nidaagwila wachimuna ni wachikazi ni kwamanga mndende. 5Mjhukulu wamkulu ni bwalo lonjhe la azee Achiyahudi akhoza kukuchimikizilani nghani izi. Kuchokela kwanyiiwo nidalandila kalata iyo idalembedwa ni wajha abale a Chiyahudi aku Damasiko, ni nidapita kujha kwaagwila wandhu ni kujhanawo ku Yelusalemu uku amangidwa maunyolo kuti alangidwe.”
Poolo wakamba umo Yesu wadamtulukila
Vichito 9:1-19; 26:12-18
6“Chimwecho yapo nidali paulendo pafupi kufika ku damasiko, ngati sasita usana chimwechi, dangalila long'azimila kupunda kuchokela kumwamba lidaniwalila kunizungulila madela yonjhe mwachizulumukila. 7Nidagwa panjhi ni nidavela mvekelo niunikambila, ‘Saulo, Saulo! Ndande yanji univuticha?’ 8Nidayangha, ‘Imwe ayani, Ambuye?’ Mvekelo udaveka, ‘Ine Yesu wa ku Nazaleti, uyo univuticha.’ 9Wandhu yawo adali niine adaliona dangalila, nambho saadauvele mvekelo wa uyo wamakamba nane. 10Ndiipo nidafunjha, ‘Ifunika nichite chiyani, Ambuye?’ Ambuye adaniyangha, ‘Ima ni upite ku Damasiko. Kumeneko sinikukambile yonjhe yayo Mnungu waikilidwa uyachite.’ 11Nidali wosapenya ndande ya lijha dangalila lalikulu lidaniwalila, ni athandizi wanga adanigwila jhanja ni kupita nane ku Damasiko.”
12“Kujha ku Damasiko kudali mundhu uyo wamatanidwa Ananiya, mundhu uyo wagwila thauko ni wamalemekezedwa ni Ayahudi wonjhe yawo amakhala ku damesiko. 13Iye wadajha kwa ine, wadaima pafupi ni ine ni kukamba, ‘Mbale wanga Saulo, penyanjho!’ Pampajha maso yanga yadayamba kupenyanjho nane nidamuona Ananiya. 14Wadakamba, ‘Mnungu wa achaatate wathu wakusangha iwe kuti ujhiwe vindu ivo avifuna uchite. Wakusangha iwe kuti umuone Mtumiki wake ni kumvela iye. 15Pakuti iwe siwakambile wandhu yajha wayaona ni kuyavela. 16Chipano siufunika kulindila ndhawi yaitali. Ima ubatizidwe ni kuelechedwa machimo yako dala ulekeleledwe kwa kukhulupilila jhina la Ambuye.’”
Ambuye amtuma Poolo kwaalalikila wandhu osati Ayahudi
17“Nidabwelela ku Yelusalemu, nambho yapo nidalikupembhela pa Nyumba ya Mnungu, nidaona masombhenya. 18Nidaaona Ambuye, uku nianikambila, ‘Uchite msanga uchoke mu Yelusalemu, pakuti wandhu anyiyawa saaulandila umboni wanga uwo siuchoche.’ 19Ine nidayangha, ‘Ambuye, anyiiwo ajhiwa bwino kuti nidapita mmanyumba yonjhe yokomanilana Ayahudi ni kwaabula yawo akukhulupililani imwe. 20Yapo wamaphedwa Sitifano mmboni wako, ine namwene nidali pampajha ni nidavomelezana kuti wapedwe niine nde nimalonda njhalu zawajha akupha’ 21Ambuye adanikambila, ‘Pita, pakuti sinikutume kutali kwa wandhu osati Ayahudi.’”
22Mbaka yapa, wajha wandhu amamvechela, nambho yapo wadakamba mawu yaya, ndiipo adakweza mvekelo wao niakamba mundhu mmeneyo waphedwe mundhu, ndande yake siwafunika kukhala wamoyo! 23Anyiiwo amabula phokoso ni kuvula njhalu zao ni kufulila lifumbi kumwamba. 24Ndiipo yujha wamkulu wa asikali wadalamula kuti amgwile Poolo ni kumlovya mkati mwa nyumba ya asikali, niwadalamula kuti wabulidwe mikwapulo, uku niwamfujha ndande yanjhi Ayahudi abula pokoso. 25Nambho yapo adathommanga vingwe kuti amkwapule, Poolo wadamfunjha mkulu wa gulu la asikali uyo wadaima pampajha pafupi ni iye, “Bwanji, thauko la jhiko la Aloma lilola kumbula mundhu wakuloma wakali osalamulidwe?”
26Wamkulu yujha yapo wadavela chimwechi, wadapita kwa wamkulu wa asikali ni kumkambila, “Ufuna kuchita chiyani? Uyu mundhu ni Mloma!”
27Chimwecho wamkulu wa asikali yujha wathamangila kwa Poolo ni kumfunjha, “Nikambile, iwe ni mundhu wa ku Loma?”
Poolo wadayangha, “Yetu, ine mundhu wa ku Loma.”
28Wamkulu wa asikali wadakamba, “Ine nane ni Mloma kwa kulipila ndalama zambili.”
Poolo wadayangha, “Nambho ine ni Mloma wobadwa.”
29Kankamojhi wandhu wajha amafuna kumfunjha uku ni ambula, pampajha adachoka ni yujha wamkulu wa asikali wadaopa kupunda yapo wadajhiwa kuti Poolo wadali Mloma wadaopa ndande wadathommanga maunyolo.
Poolo wapelekedwa pa bwalo la milandu
30Siku lakawili wamkulu wa asikali wamafuna kujhiwa ndande iyo Ayahudi amafuna kumpacha mlandu Poolo. Chimwecho wadammasula yajha maunyolo ni wadalamula ajhukulu wakulu na azee a bwalo lalikulu lonjhe kukomana pamojhi. Ndiipo wadamtenga Poolo ni kumuika waime pachogolo pao.
ទើបបានជ្រើសរើសហើយ៖
:
គំនូសចំណាំ
ចែករំលែក
ចម្លង
ចង់ឱ្យគំនូសពណ៌ដែលបានរក្សាទុករបស់អ្នក មាននៅលើគ្រប់ឧបករណ៍ទាំងអស់មែនទេ? ចុះឈ្មោះប្រើ ឬចុះឈ្មោះចូល
The New Testament in Nyanja @The Word for The World International and Nyanja Language translation, 2025. All rights reserved.