Vichito 2:2-4
Vichito 2:2-4 NTNYBL2025
Mwachizulumukila mvekelo waukulu ngati mkokomo wa mbhepo udachoka kumwamba ni kuijhaza nyumba yonjhe mujha adakhala wajha atumwi. Kudatulukila malilime ya moto yayo yadagawika ni kukhala pamwamba pa kila mmojhi wawo. Wandhu wonjhe adajhazidwa ni Mzimu Woyela, adayamba kukamba mikambo ya chilendo, ngati umo wadafunila Mzimu Woyela.


