“Mkhale maso ni woyaluza amathauko. Anyiiwo akonda kuyendayenda uku avalila makhanzu yayatali. Yawo akonda kulonjeledwa mmalo yayo akomana wandhu ambili, ni anyiyawo akonda kukhala mmipando ya pachogolo mnyumba za mapembhelo, ni kukonda kukhala mipando ya ulemu mmaphwando. Yawo atenga chuma cha wachikazi yawo afedwa ni achamunawo ni kupembhela mapembhelo yayatali, kuti awonekane kuti ni abwino pamaso pa wandhu. Wandu ngati achamenecho, salamulidwe kupunda.”