1
Vichito 13:2-3
Nyanja
NTNYBL2025
Yapo amampembha Mnungu ni kumanga kudya, Mzimu Woyela udaakambila, “Nipatulileni Banaba ni Saulo, kuti achite njhito iyo naatanila kuchita.” Yapo adamaliza kumanga kudya ni kupembhela, anyiiwo adaasanjika manja Banaba ni Saulo ni kwasiya ajhipita.
ប្រៀបធៀប
រុករក Vichito 13:2-3
2
Vichito 13:39
Mundhu waliyonjhe uyo wamkhulupilila Kilisito siwalekeleledwe machimo yake. Chindhu icho sichidakakhozeka kwa kulemekeza thauko la Musa.
រុករក Vichito 13:39
3
Vichito 13:47
Ili nde lamulo ilo atipacha Ambuye, ‘Nakuchitani kukhala dangalila kwa wandhu osati Ayahudi, kuti wandhu onjhe ajhiko la panjhi aomboledwe.’”
រុករក Vichito 13:47
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ