Mk. 5:25-26

Mk. 5:25-26 BLY-DC

Tsono panali mai wina amene adakhala akuvutika ndi matenda a msambo pa zaka khumi ndi ziŵiri. Adaazunzika zedi ndi asing'anga ochuluka amene ankayesa kumuchiza. Mwakuti adaamwaza chuma chake chonse, komabe osapeza bwino konse. M'malo mwake matendawo analikunka nakulirakulira.

مطالعه Mk. 5

ویدیوهای مرتبط

برنامه های خواندنی رایگان و عبادات مربوط به Mk. 5:25-26