Mk. 2:12

Mk. 2:12 BLY-DC

Munthu uja adadzukadi, natenga machira ake aja nkutuluka, onse aja akuwona. Anthu onse aja adazizwa kwambiri, nayamba kutamanda Mulungu nkumanena kuti, “Zoterezi ife sitinaziwone nkale lonse.”

مطالعه Mk. 2

ویدیوهای مرتبط

برنامه های خواندنی رایگان و عبادات مربوط به Mk. 2:12