YouVersion Logo
Search Icon

2 AKORINTO 4:16-17

2 AKORINTO 4:16-17 BLPB2014

Chifukwa chake sitifooka; koma ungakhale umunthu wathu wakunja uvunda, wa m'kati mwathu ukonzedwa kwatsopano tsiku ndi tsiku. Pakuti chisautso chathu chopepuka cha kanthawi chitichitira ife kulemera koposa kwakukulu ndi kosatha kwa ulemerero

Free Reading Plans and Devotionals related to 2 AKORINTO 4:16-17