1
Matayo 27:46
Nyanja
NTNYBL2025
Yapo idafika saa tisa, Yesu wadakweza mvekelo, “Eloi, Eloi, lama sabakitani?” Mate yake, “Mnungu wanga, Mnungu wanga, mbona mwanisiya?”
Compare
Explore Matayo 27:46
2
Matayo 27:51-52
Pampajh, panzia ilo lidapachikidwa mnyumba ya Mnungu, lidang'ambika pakati kuyambila kumwamba mbaka panjhi. Jhiko lidatingizika ni ndhaka idasweka, viliza vidamasuka, ni wandhu ambili a Mnungu yawo adamwalila, adahyuka.
Explore Matayo 27:51-52
3
Matayo 27:50
Yesu wadatananjho kwa mvekelo waukulu, wadamwalila.
Explore Matayo 27:50
4
Matayo 27:54
Yujha wamkulu wa asikali, pamojhi ni asikali yawo amalonda chiliza cha Yesu, yapo adaona chimtingiza cha ndhaka ni kila kandhu yako kadachitika, adagwilidwa ni mandha, adakamba, “Zenedi, uyu wadali Mwana wa Mnungu!”
Explore Matayo 27:54
5
Matayo 27:45
Kuchokela saa sita mbaka sa tisa usana, mdima udavinikila jhiko lonjhe.
Explore Matayo 27:45
6
Matayo 27:22-23
Pilato wadafunjha, “Nimchite chiyani uyu Yesu watanidwa Kilisito?” Onjhe adakamba “Wapachikidwe pamtanda!” Pilato wadaafunjha, “Ndande yanji? Wachita chindhu chanji choipa?” Adamkambila “Mpachikeni pamtanda!”
Explore Matayo 27:22-23
Home
Bible
Plans
Videos