1
1 AKORINTO 8:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
koma kwa ife kuli Mulungu mmodzi, Atate amene zinthu zonse zichokera kwa Iye, ndi ife kufikira kwa Iye; ndi Ambuye mmodzi Yesu Khristu, amene zinthu zonse zili mwa Iye, ndi ife mwa Iye.
Compare
Explore 1 AKORINTO 8:6
2
1 AKORINTO 8:1-2
Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira. Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa.
Explore 1 AKORINTO 8:1-2
3
1 AKORINTO 8:13
Chifukwa chake, ngati chakudya chikhumudwitsa mbale wanga, sindidzadya nyama kunthawi yonse, kuti ndingakhumudwitse mbale wanga.
Explore 1 AKORINTO 8:13
4
1 AKORINTO 8:9
Koma yang'anirani kuti ulamuliro wanu umene ungakhale chokhumudwitsa ofookawo.
Explore 1 AKORINTO 8:9
Home
Bible
Plans
Videos