YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 8:1-2

1 AKORINTO 8:1-2 BLPB2014

Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira. Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa.