1
1 AKORINTO 7:5
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Musakanizana, koma ndi kuvomerezana kwanu ndiko, kwa nthawi, kuti mukadzipereke kwa kupemphera, nimukakhalenso pamodzi, kuti Satana angakuyeseni, chifukwa cha kusadziletsa kwanu.
Compare
Explore 1 AKORINTO 7:5
2
1 AKORINTO 7:3-4
Mwamunayo apereke kwa mkazi mangawa ake; koma modzimodzinso mkazi kwa mwamuna. Mkazi alibe ulamuliro wa pa thupi lake la iye yekha, koma mwamuna ndiye; koma momwemonso mwamuna alibe ulamuliro wa pa thupi la iye yekha, koma mkazi ndiye.
Explore 1 AKORINTO 7:3-4
3
1 AKORINTO 7:23
Munagulidwa ndi mtengo wake; musakhale akapolo a anthu.
Explore 1 AKORINTO 7:23
Home
Bible
Plans
Videos