Biểu trưng YouVersion
Biểu tượng Tìm kiếm

Genesis 3:17

Genesis 3:17 CCL

Ndipo kwa Adamu Mulungu anati, “Chifukwa wamvera mkazi wako ndipo wadya zipatso za mu mtengo umene ndinakulamulira kuti, ‘Usadye.’ “Nthaka yatembereredwa chifukwa cha iwe, movutikira udzadya zochokera mʼnthakamo masiku onse a moyo wako.

Những video dành cho Genesis 3:17

Các Kế hoạch Đọc và Tĩnh nguyện miễn phí liên quan đếnGenesis 3:17