1
2 AKORINTO 7:10
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti chisoni cha kwa Mulungu titembenuzira mtima kuchipulumutso, chosamvetsanso chisoni; koma chisoni cha dziko lapansi chichita imfa.
Linganisha
Chunguza 2 AKORINTO 7:10
2
2 AKORINTO 7:1
Pokhala nao tsono malonjezano amenewa, okondedwa, tidzikonzere tokha kuleka chodetsa chonse cha thupi ndi cha mzimu, ndi kutsiriza chiyero m'kuopa Mulungu.
Chunguza 2 AKORINTO 7:1
3
2 AKORINTO 7:9
Tsopano ndikondwera, si kuti mwangomvedwa chisoni, koma kuti mwamvetsedwa chisoni ku kutembenuka mtima; pakuti munamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, kuti tisakusowetseni m'kanthu kalikonse.
Chunguza 2 AKORINTO 7:9
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video