1
2 AKORINTO 8:9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti mudziwa chisomo cha Ambuye wathu Yesu Khristu, kuti, chifukwa cha inu anakhala wosauka, angakhale anali wolemera, kuti inu ndi kusauka kwake mukakhale olemera.
Linganisha
Chunguza 2 AKORINTO 8:9
2
2 AKORINTO 8:2
kuti m'chitsimikizo chachikulu cha chisautso, kuchulukitsa kwa chimwemwe chao, ndi kusauka kwao, kwenikweni zidachulukira ku cholemera cha kuolowa mtima kwao.
Chunguza 2 AKORINTO 8:2
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video