Vichito 7:59-60
Vichito 7:59-60 NTNYBL2025
Yapo amaendekela kumpmonya miyala, Sitifano wadapembhela, “Ambuye Yesu, landilani mzimu wanga!” Wadagwada ni kulila kwa mvekelo wa waukulu, “Ambuye, musadalamula wandhu yawa kwa machimo yaya.” Yapo wadamaliza kukamba chimwecho, wadamwalila.

