Yapo wadamaliza kukamba yameneyo, wadatana kwa mvekelo waukulu, “Lazalo, majha kuno kubwalo!” Yujha wadamwalila wadatuluka kubwalo, wali omangidwa sanda mmyendo ni mmanja, ni kumaso wavinikilidwa njhalu.
Yesu wadakambila, “Mmasuleni, mumsiye wajhipita.”