1
EKSODO 29:45-46
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ndidzakhala pakati pa ana a Israele, ndi kukhala Mulungu wao. Ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao, amene ndinawatulutsa m'dziko la Ejipito, kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Yehova Mulungu wao.
ប្រៀបធៀប
រុករក EKSODO 29:45-46
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ