ឡូហ្គូ YouVersion
ព្រះគម្ពីរគម្រោងអានវីដេអូ
ទាញយកកម្មវិធី
ជម្រើសភាសា
អាយខន ស្វែង​រក

ខគម្ពីរពេញនិយមពី Genesis 7

1

Genesis 7:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova anati kwa Nowa, “Lowa mu chombo iwe ndi banja lako lonse, chifukwa ndaona kuti ndiwe wolungama mu mʼbado uwu.

ប្រៀបធៀប

រុករក Genesis 7:1

2

Genesis 7:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.

ប្រៀបធៀប

រុករក Genesis 7:24

3

Genesis 7:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pa tsiku la 17 la mwezi wachiwiri, Nowa ali ndi zaka 600, akasupe onse akuya kwambiri anasefuka ndiponso zitseko za madzi akumwamba zinatsekuka.

ប្រៀបធៀប

រុករក Genesis 7:11

4

Genesis 7:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chamoyo chilichonse pa dziko lapansi chinawonongedwa, kuyambira munthu, nyama, zokwawa ndi mbalame. Nowa yekha ndiye anatsala pamodzi ndi onse amene anali naye.

ប្រៀបធៀប

រុករក Genesis 7:23

5

Genesis 7:12

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo mvula inagwa pa dziko lapansi masiku makumi anayi usana ndi usiku.

ប្រៀបធៀប

រុករក Genesis 7:12

ជំពូកមុន
ជំពូកបន្ទាប់
YouVersion

ទទួលការលើកទឹកចិត្តនិងជំរុញឱ្យអ្នកស្វែងរកភាពស្និទ្ធស្នាលជាមួយនឹងព្រះជាម្ចាស់ជាប្រចាំថ្ងៃ។

ព័ន្ធកិច្ច

អំពី

អាជីព

អ្នកស្ម័គ្រចិត្ត

ប្លុកសារ

ដំណឹង

តំណមានប្រយោជន៍

ជំនួយ

បរិច្ចាគ

ជំនាន់​ព្រះ​គម្ពីរ

ព្រះគម្ពីរជាសំឡេង

ភាសា​ព្រះ​គម្ពីរ

ខគម្ពីរ​សម្រាប់​ថ្ងៃ​នេះ


ព័ន្ធកិច្ចបែបឌីជីថលរបស់

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

គោលការណ៍ច្បាប់ឯកជនលក្ខខណ្ឌ
កម្មវិធីបង្ហាញពីភាពងាយរងគ្រោះ
ហ្វេសប៊ុកTwitterអ៊ីនស្ដាក្រាមយូធូបPinterest

គេហ៍

ព្រះគម្ពីរ

គម្រោងអាន

វីដេអូ