1
Genesis 10:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
ប្រៀបធៀប
រុករក Genesis 10:8
2
Genesis 10:9
Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”
រុករក Genesis 10:9
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ