Mk. 13:24-25
Mk. 13:24-25 BLY-DC
“Masiku amenewo, mavutowo atatha, dzuŵa lidzada, mwezi udzaleka kuŵala. Nyenyezi zidzagwa kuchokera ku thambo, ndipo mphamvu zamumlengalenga zidzagwedezeka.
“Masiku amenewo, mavutowo atatha, dzuŵa lidzada, mwezi udzaleka kuŵala. Nyenyezi zidzagwa kuchokera ku thambo, ndipo mphamvu zamumlengalenga zidzagwedezeka.