لوگو یوورژن
كتاب‌ مقدسبرنامه‌های مطالعهویدیوها
دانلود برنامه
انتخاب زبان
ایکن جستجو

آیات محبوب کتاب مقدس از MACHITIDWE 16

1

MACHITIDWE 16:31

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo iwo anati, Ukhulupirire Ambuye Yesu, ndipo udzapulumuka, iwe ndi apabanja ako.

مقایسه

MACHITIDWE 16:31 را جستجو کنید

2

MACHITIDWE 16:25-26

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma ngati pakati pa usiku, Paulo ndi Silasi analinkupemphera, naimbira Mulungu nyimbo, ndipo a m'ndendemo analinkuwamva; ndipo mwadzidzidzi panali chivomezi chachikulu, chotero kuti maziko a ndende anagwedezeka: pomwepo pamakomo ponse panatseguka; ndi maunyolo a onse anamasuka.

مقایسه

MACHITIDWE 16:25-26 را جستجو کنید

3

MACHITIDWE 16:30

Buku Lopatulika

BLP-2018

nawatulutsira iwo kunja, nati, Ambuye, ndichitenji kuti ndipulumuke?

مقایسه

MACHITIDWE 16:30 را جستجو کنید

4

MACHITIDWE 16:27-28

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pamene anautsidwa kutulo mdindoyo, anaona kuti pa makomo a ndende panatseguka, ndipo anasolola lupanga lake, nati adziphe yekha, poyesa kuti am'ndende adathawa. Koma Paulo anafuula ndi mau aakulu, nati, Usadzipweteka wekha; tonse tili muno.

مقایسه

MACHITIDWE 16:27-28 را جستجو کنید

باب‌ قبلی
باب بعدی
یوورژن

به چالش کشیدن و تشویق هر روزه شما برای ایجاد رابطه صمیمی تر با خدا .

خدمت

دربارهٔ

مشاغل

داوطلب شوید.

بلاگ

مطبوعات

لینک‌های مفید

پشتیبانی

اهدای کمک مالی

ترجمه‌های کتاب‌مقدس

کتاب‌ مقدس صوتی

ترجمه‌های موجود کتاب‌مقس

آیۀ روز


یک خدمت دیجیتالی از

لایف‌چرچ
فارسی

©2026 لایف چرچ / یوورژن

قوانین حفظ حریم شخصیشرايط
برنامه افشای آسیب پذیری
فیس‌بوکتویتراینستاگرامبرنامه یوتیوببرنامه پین ترست