YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 2:11

MATEYU 2:11 BLPB2014

Ndipo pofika kunyumba anaona kamwanako ndi Maria amake, ndipo anagwa pansi namgwadira Iye; namasula chuma chao, nampatsa Iye mitulo, ndiyo golide ndi lubani ndi mure.