YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 39:6

Yesaya 39:6 CCL

Yehova akuti, nthawi idzafika ndithu pamene zonse za mʼnyumba mwanu ndi zonse zimene makolo anu anazisonkhanitsa mpaka lero lino, zidzatengedwa kupita nazo ku Babuloni. Sipadzatsalapo ndi kanthu kamodzi komwe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 39:6