1
Mt. 4:4
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Koma Yesu adati, “Malembo akuti, “ ‘Munthu sangakhale moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mau onse olankhula Mulungu.’ ”
Compare
Explore Mt. 4:4
2
Mt. 4:10
Apo Yesu adati, “Choka, Satana! Paja Malembo akuti, ‘Uzipembedza Ambuye, Mulungu wako, ndipo uziŵatumikira Iwo okha.’ ”
Explore Mt. 4:10
3
Mt. 4:7
Koma Yesu adati, “Malembo akutinso, ‘Usaŵayese Ambuye, Mulungu wako.’ ”
Explore Mt. 4:7
4
Mt. 4:1-2
Zitatha izi, Mzimu Woyera adatsogolera Yesu kupita ku chipululu kuti Satana akamuyese. Pa masiku makumi anai Yesu adasala zakudya usana ndi usiku, ndipo pambuyo pake adamva njala.
Explore Mt. 4:1-2
5
Mt. 4:19-20
Yesu adaŵauza kuti, “Inu, munditsate, ndikakusandutseni asodzi a anthu.” Pomwepo iwo adasiya makoka ao, namamtsatadi.
Explore Mt. 4:19-20
6
Mt. 4:17
Kuyambira nthaŵi imeneyo Yesu adayamba kulalika kuti, “Tembenukani mtima, chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.”
Explore Mt. 4:17