1
Mt. 3:8
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Chitanitu ntchito zosonyeza kuti mwatembenukadi mtima.
Compare
Explore Mt. 3:8
2
Mt. 3:17
Tsono kuthamboko kudamveka mau akuti, “Uyu ndiye Mwana wanga wapamtima. Ndimakondwera naye kwambiri.”
Explore Mt. 3:17
3
Mt. 3:16
Yesu atangobatizidwa, adatuluka m'madzimo. Pomwepo kuthambo kudatsekuka, ndipo adaona Mzimu wa Mulungu akutsika ngati nkhunda nkutera pa Iye.
Explore Mt. 3:16
4
Mt. 3:11
“Ine ndimakubatizani ndi madzi, kusonyeza kuti mwatembenuka mtima. Koma amene akubwera pambuyo panga ndi wamphamvu kuposa ine. Ameneyo ine ndine wosayenera ngakhale kunyamula nsapato zake. Iyeyo adzakubatizani mwa Mzimu Woyera ndiponso m'moto.
Explore Mt. 3:11
5
Mt. 3:10
Pali pano nkhwangwa ili kale patsinde pa mitengo. Choncho mtengo uliwonse wosabala zipatso zabwino, adzaudula nkuuponya pa moto.
Explore Mt. 3:10
6
Mt. 3:3
Paja Yesaya ankanena za iyeyu pamene adaati, “Liwu la munthu wofuula m'chipululu: akunena kuti, ‘Konzani mseu wodzadzeramo Ambuye, ongolani njira zoti adzapitemo.’ ”
Explore Mt. 3:3