1
HOSEYA 13:4
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma Ine ndiye Yehova Mulungu wako chichokere m'dziko la Ejipito, ndipo suyenera kudziwa mulungu wina koma Ine; ndi popanda Ine palibe mpulumutsi.
Compare
Explore HOSEYA 13:4
2
HOSEYA 13:14
Ndidzawaombola kumphamvu ya kumanda, ndidzawaombola kuimfa; imfa, miliri yako ili kuti? Kulekerera kudzabisika pamaso panga.
Explore HOSEYA 13:14
3
HOSEYA 13:6
Monga mwa podyetsa pao, momwemo anakhuta; anakhuta, ndi mtima wao unakwezeka; chifukwa chake anandiiwala Ine.
Explore HOSEYA 13:6