1
HOSEYA 14:9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Wanzeru ndani, kuti azindikire izi? Waluntha, kuti adziwe izi? Pakuti njira za Yehova zili zoongoka; ndipo olungama adzayendamo, koma olakwa adzagwamo.
Compare
Explore HOSEYA 14:9
2
HOSEYA 14:2
Mukani nao mau, nimubwerere kwa Yehova; nenani kwa Iye, Chotsani mphulupulu zonse, nimulandire chokoma; ndipo tidzapereka mau milomo yathu ngati ng'ombe.
Explore HOSEYA 14:2
3
HOSEYA 14:4
Ndidzachiritsa kubwerera kwao, ndidzawakonda mwaufulu; pakuti mkwiyo wanga wamchokera.
Explore HOSEYA 14:4