1
1 AKORINTO 14:33
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
pakuti Mulungu sali Mulungu wa chisokonezo koma wa mtendere; monga mwa Mipingo yonse ya oyera mtima.
Compare
Explore 1 AKORINTO 14:33
2
1 AKORINTO 14:1
Tsatani chikondi; koma funitsitsani mphatso zauzimu, koma koposa kuti mukanenere.
Explore 1 AKORINTO 14:1
3
1 AKORINTO 14:3
Koma iye wakunenera alankhula ndi anthu chomangirira ndi cholimbikitsa, ndi chosangalatsa.
Explore 1 AKORINTO 14:3
4
1 AKORINTO 14:4
Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.
Explore 1 AKORINTO 14:4
5
1 AKORINTO 14:12
Momwemo inunso, popeza muli ofunitsitsa mphatso za Mzimu, funani kuti mukachuluke kukumangirira kwa Mpingo.
Explore 1 AKORINTO 14:12
Home
Bible
Plans
Videos