1
Nyimbo ya Solomoni 8:6
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 8:6
2
Nyimbo ya Solomoni 8:7
Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, mitsinje singachikokolole chikondicho. Ngati wina apereka chuma chonse cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu.
Explore Nyimbo ya Solomoni 8:7