1
Nyimbo ya Solomoni 5:16
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri; munthuyo ndi wokongola kwambiri! Uyu ndiye wachikondi wanga ndi bwenzi langa, inu akazi a ku Yerusalemu.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 5:16
2
Nyimbo ya Solomoni 5:10
Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzi pakati pa anthu 1,000.
Explore Nyimbo ya Solomoni 5:10