1
Nyimbo ya Solomoni 4:7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndiwe wokongola kwambiri wokondedwa wanga; palibe chilema pa iwe.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 4:7
2
Nyimbo ya Solomoni 4:9
Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, wanditenga mtima, iwe wanditenga mtima ndi kapenyedwe ka maso ako, ndiponso ndi umodzi mwa mikanda ya mʼkhosi mwako.
Explore Nyimbo ya Solomoni 4:9