1
Nyimbo ya Solomoni 6:3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga; amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 6:3
2
Nyimbo ya Solomoni 6:10
Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha, wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa, wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?
Explore Nyimbo ya Solomoni 6:10