1
Nyimbo ya Solomoni 3:1
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Usiku wonse ndili pa bedi langa ndinafunafuna amene mtima wanga umamukonda; ndinamufunafuna koma osamupeza.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 3:1
2
Nyimbo ya Solomoni 3:2
Ndikudzuka tsopano ndipo ndidzayendayenda mu mzinda, mʼmisewu yake ndi mʼmabwalo ake; ndidzamufunafuna amene mtima wanga umamukonda. Kotero ine ndinamufunafuna iyeyo koma osamupeza.
Explore Nyimbo ya Solomoni 3:2