1
Nyimbo ya Solomoni 2:10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine, “Dzuka bwenzi langa, wokongola wanga, ndipo tiye tizipita.
Compare
Explore Nyimbo ya Solomoni 2:10
2
Nyimbo ya Solomoni 2:16
Bwenzi langa ndi wangadi ndipo ine ndine wake; amadyetsa gulu lake la ziweto pakati pa maluwa okongola.
Explore Nyimbo ya Solomoni 2:16