1
Miyambo 25:28
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Munthu amene samatha kudziretsa ali ngati mzinda umene adani awuthyola ndi kuwusiya wopanda malinga.
Compare
Explore Miyambo 25:28
2
Miyambo 25:21-22
Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye; ngati ali ndi ludzu mupatse madzi kuti amwe. Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake, ndipo Yehova adzakupatsa mphotho.
Explore Miyambo 25:21-22