1
Mateyu 10:16
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Taonani ndikukutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu. Chifukwa chake khalani ochenjera ngati njoka ndi woona mtima ngati nkhunda.
Compare
Explore Mateyu 10:16
2
Mateyu 10:39
Aliyense amene asunga moyo wake adzawutaya koma aliyense amene ataya moyo chifukwa cha Ine adzawupeza.
Explore Mateyu 10:39
3
Mateyu 10:28
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena.
Explore Mateyu 10:28
4
Mateyu 10:38
Aliyense amene satenga mtanda wake ndi kunditsata Ine sayenera kukhala wanga.
Explore Mateyu 10:38
5
Mateyu 10:32-33
“Aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzavomereza pamaso pa Atate anga akumwamba. Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamukana pamaso pa Atate anga akumwamba.
Explore Mateyu 10:32-33
6
Mateyu 10:8
Chiritsani odwala, ukitsani akufa, chiritsani akhate, tulutsani ziwanda. Munalandira kwaulere, perekani kwaulere.
Explore Mateyu 10:8
7
Mateyu 10:31
Potero musaope; inu ndinu a mtengo woposa mbalame zambiri.
Explore Mateyu 10:31
8
Mateyu 10:34
“Musaganize kuti Ine ndabweretsa mtendere pa dziko lapansi. Sindinabwere kudzapereka mtendere koma lupanga.
Explore Mateyu 10:34