1
Mateyu 9:37-38
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Pamenepo anati kwa ophunzira ake, “Zokolola ndi zambiri koma antchito ndi ochepa. Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.”
Compare
Explore Mateyu 9:37-38
2
Mateyu 9:13
Koma pitani kaphunzireni tanthauzo la mawu awa: ‘Ndimafuna chifundo osati nsembe ayi.’ Pakuti sindinabwere kudzayitana olungama koma ochimwa.”
Explore Mateyu 9:13
3
Mateyu 9:36
Ataona maguluwo, anagwidwa ndi chisoni chifukwa anali ozunzika ndi osowa chithandizo ngati nkhosa zopanda mʼbusa.
Explore Mateyu 9:36
4
Mateyu 9:12
Yesu atamva, anati, “Munthu wamoyo safuna singʼanga ayi, koma wodwala.
Explore Mateyu 9:12
5
Mateyu 9:35
Yesu anayendayenda mʼmizinda yonse ndi mʼmidzi, kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa nthenda zawo zonse ndi zofowoka za mʼmatupi mwawo.
Explore Mateyu 9:35