1
Mateyu 11:28
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo.
Compare
Explore Mateyu 11:28
2
Mateyu 11:29
Senzani goli langa ndipo phunzirani kwa Ine, pakuti ndine wofatsa ndi wodzichepetsa. Ndipo inu mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.
Explore Mateyu 11:29
3
Mateyu 11:30
Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka.”
Explore Mateyu 11:30
4
Mateyu 11:27
“Zinthu zonse zapatsidwa kwa Ine ndi Atate anga. Palibe mmodzi amene adziwa Mwana kupatula Atate ndipo palibe mmodzi amene adziwa Atate kupatula Mwana ndi kwa iwo amene Mwana awasankha kuwawululira.
Explore Mateyu 11:27
5
Mateyu 11:4-5
Yesu anayankha kuti, “Bwererani ndi kukamuwuza Yohane zimene mwamva ndi kuona. Osaona akuona, olumala akuyenda, akhate akuchiritsidwa, osamva akumva, akufa akuukitsidwa ndipo Uthenga Wabwino ukulalikidwa kwa osauka.
Explore Mateyu 11:4-5
6
Mateyu 11:15
Iye amene ali ndi makutu amve.
Explore Mateyu 11:15