1
Ezekieli 21:27
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Chipasupasu! Chipasupasu! Ine ndidzawupasula mzindawo! Ndipo sadzawumanganso mpaka atafika amene ali woyenera kuwulandira; Ine ndidzawupereka kwa iyeyo.’
Compare
Explore Ezekieli 21:27
2
Ezekieli 21:26
Ambuye Yehova akuti: Vula nduwira, chotsa chipewa chaufumu. Zinthu sizidzakhala monga zinalili: anthu wamba adzakwezedwa ndipo okwezedwa adzatsitsidwa.
Explore Ezekieli 21:26