1
Ezekieli 22:30
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Ndinafunafuna munthu pakati pawo woti amange linga, woti ayimirire dziko pamaso panga kundipepesa kuti ndisaliwononge, koma sindinamupeze.
Compare
Explore Ezekieli 22:30
2
Ezekieli 22:31
Nʼchifukwa chake ndawakwiyira kwambiri. Ndawawonongeratu ndi mkwiyo wanga woyaka ngati moto. Ndawalanga molingana ndi zimene anachita. Akutero Ambuye Yehova.”
Explore Ezekieli 22:31