1
Ezekieli 20:20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Masabata anga muziwasunga ngati opatulika kuti akhale chizindikiro pakati pa Ine ndi inu. Mukatero mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’
Compare
Explore Ezekieli 20:20
2
Ezekieli 20:19
Ine ndine Yehova Mulungu wanu; tsatirani malangizo anga ndipo sungani malamulo anga.
Explore Ezekieli 20:19