1
Ezekieli 14:6
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Nʼchifukwa chake uwawuze Aisraeli kuti Ine Ambuye Yehova ndikuti: Lapani! Siyani mafano anu ndi ntchito zanu zonse zonyansa!
Compare
Explore Ezekieli 14:6
2
Ezekieli 14:5
Ine ndidzachita zimenezi kuti mwina nʼkukopa mitima ya anthu a Israeli, amene andisiya chifukwa cha mafano awo.’
Explore Ezekieli 14:5